” Eee inu amene mwakhulupilira,zitetezeni nokha pamodzi ndi mabanja anu Ku ng’anjo ya moto umene nkhuni zake ndi anthu komanso miyala,omwe ayang’aniri ake ndi Angelo owoopsa ndi amphamvu,ndipo samanyonzera zomwe Allah awalamura,iwo amachita zomwe Allah awalamura (Al-qur’an 66/6). Mthenga wa Allah madalitso ndi mtendere zipite kwa iye adati; “Mwana ariyense …
Read More »Katemera
DOWNLOAD
Read More »Sunnah of Musaafahah – Chichewa
Asilamu awiri atakumana. Patatha miyedzi iwiri kapena itatu mu lock down. Zoona zake ndi chisangalaro komanso chikodwelero ndiye nkhani ndiyakuti kugwirana manja wina ndi mnzake monga mmene machitidwe amtumiki wathu ( Sallalahu alayhi wa sallam) sunnah. Monga omutsatira masahaba Radhiyallahu anhum amkachitira. Nthawi iti! Nthawi pamene, Munthu wina ndi mnzake …
Read More »